Genesis 25:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo maina a ana a Ismayeli, maina ao m'mibadwo yao ndi awa: woyamba wa Ismayeli ndi Nebayoti; ndi Kedara, ndi Abideele, ndi Mibisamu,

Genesis 25

Genesis 25:3-22