Genesis 24:25-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

25. Natinso kwa iye, Tiri nao maudzu ndi zakudya zambiri oeli malo ogona.

26. Munthuyo oelipo anawerama mutu namyamika Yehova.

27. Ndipo anati, Ayamikike Yehova Mulungu wa mbuyanga Abrahamuamene sanasiya mbuyanga wopanda cifundo cace ndi zoona zace: koma ine Yehova Wanditsogolera m'njira ya ku nyumba ya abale ace a mbuyanga.

28. Namwaliyo ndipo anathamanga nawauza zimenezo ku nyumba ya amace.

Genesis 24