Genesis 20:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma Mulungu anadza kwa Abimeleke m'kulota kwa usiku, nati kwa iye, Taona, wakufa iwe, cifukwa ca mkazi amene wamtenga: pakuti iye ndiye mkazi wa mwini.

Genesis 20

Genesis 20:1-9