Genesis 10:24-30 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

24. Aripakasadi ndipo anabala Sela; ndipo Sela anabala Ebere.

25. Kwa Ebere ndipo kunabadwa ana amuna awiri; dzina la wina ndi Pelege; cifukwa kuti m'masiku ace dziko lapansi linagawanikana; dzina la mphwace ndi Yokitani.

26. Ndipo Yokitani anabala Alamodadi, ndi Selefe, ndi Hazaramaveti, ndi Yera;

27. ndi Hadorimu ndi Uzali, ndi Dikila;

28. ndi Obali, ndi Abimaele, ndi Sheva;

29. ndi Ofiri ndi Havila, ndi obabi; onse amenewa ndi ana a okitani.

30. Kwao kunayamba pa Mesa pakunka ku Sefere phiri la kum'mawa.

Genesis 10