Ezekieli 7:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo akupulumuka mwa iwo adzapulumuka, koma adzakhala kumapiri ngati njiwa za kuzigwa, onse akubuula, ali yense m'mphulupulu zace.

Ezekieli 7

Ezekieli 7:13-18