Ezekieli 7:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo mau a Yehova anandidzera, akuti,

2. Ndipo iwe wobadwa ndi munthu, atero Ambuye Yehova kwa dziko la Israyeli, Kwatha; kwafika kutha kwace pa ngondya zinai za dziko.

3. Tsopano kwakudzera kutha kwako, ndipo ndidzakutumizira mkwiyo wanga, ndi kukuweruza monga mwa njira zako, ndipo ndidzakubwezera zonyansa zako zanse.

Ezekieli 7