Ezekieli 6:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi maguwa anu a nsembe adzakhala opasuka, ndi zoimiritsa zanu zadzuwa zidzasweka; ndipo ndidzagwetsa ophedwa anu pamaso pa mafano anu.

Ezekieli 6

Ezekieli 6:1-12