Ezekieli 5:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma anakaniza maweruzo anga ndi kucita zoipa koposa amitundu, nakaniza malemba anga koposa maiko akuuzungulira; pakuti anataya maweruzo anga, ndi malemba anga, sanayendamo.

Ezekieli 5

Ezekieli 5:5-11