Ezekieli 47:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anaturuka nane njira ya ku cipata ca kumpoto, nazungulira nane njira yakunja kumka ku cipata cakunja, njira ya ku cipata coloza kum'mawa; ndipo taonani, panaturuka madzi pa mbali ya kulamanja.

Ezekieli 47

Ezekieli 47:1-7