Ezekieli 45:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo zikwi makumi awiri mphambu zisanu m'litali mwace, ndi zikwi khumi kupingasa kwace, ndilo gawo la Alevi, atumiki a kacisi; likhale lao lao la midzi yokhalamo.

Ezekieli 45

Ezekieli 45:4-12