Ezekieli 44:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Atero Ambuye Yehova, Palibe mlendo wosadulidwa m'mtima, wosadulidwa m'thupi, alowe m'malo anga opatulika, mwa alendo onse ali pakati pa ana a Israyeli.

Ezekieli 44

Ezekieli 44:1-11