Ezekieli 41:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anayesa khoma la nyumba, kucindikira kwace mikono isanu ndi umodzi, ndi kupingasa kwace kwa zipinda za m'mphepete mikono inai, pozungulira pace ponse pa kacisi.

Ezekieli 41

Ezekieli 41:3-13