Ezekieli 41:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panalembedwa pamenepo pa Izitseko za Kacisi akerubi ndi akanjedza, akunga aja adalembedwa pamakhoma; ndipo panali matabwa ocindikira pakhomo pakhonde panja,

Ezekieli 41

Ezekieli 41:18-26