Ezekieli 40:48 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anadza nane ku khonde la kacisi, nayesa mphuthu za khonde, mikono isanu cakuno, ndi mikono isanu cauko; ndi kupingasa kwa cipata, mikono itatu cakuno, ndi mikono itatu cauko.

Ezekieli 40

Ezekieli 40:45-49