Ezekieli 40:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo analowa nane ku bwalo lakunja, ndipo taonani, panali zipinda, ndi moyalidwa miyala mokonzekera bwalo pozungulira ponse; moyalidwa miyalamo munali zipinda makumi atatu.

Ezekieli 40

Ezekieli 40:15-19