Ezekieli 39:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adzasankha anthu akupita-pitabe m'dziko, ndi pamodzi ndi opitapitawo anthu akuika mafupa otsala pamtunda, kuliyeretsa; pakutha miyezi isanu ndi iwiri adzapwaira.

Ezekieli 39

Ezekieli 39:10-24