Ezekieli 38:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ndanena mu nsanje yanga, ndi m'moto wa kuzaza kwanga, Zoonadi tsiku ilo kudzakhala kugwedezeka kwakukuru m'dziko la Israyeli;

Ezekieli 38

Ezekieli 38:14-22