Ezekieli 37:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo ndidzawayesa mtundu umodzi m'dzikomo, pa mapiri a Israyeli; ndipo mfumu imodzi idzakhala mfumu ya iwo onse, sadzakhalanso mitundu iwiri, kapena kugawanikanso maufumu awiri konse ai.

Ezekieli 37

Ezekieli 37:16-28