Ezekieli 32:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma sagona pamodzi ndi amphamvu osadulidwa adagwawo amene anatsikira kumanda ndi zida zao za nkhondo, amene anawatsamiritsa malupanga ao; ndi mphulupulu zao ziri pa mafupa ao; pakuti anaopsetsa amphamvu m'dziko la amoyo.

Ezekieli 32

Ezekieli 32:23-32