Ezekieli 27:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuturuka malonda ako m'nyanja unadzaza mitundu yambiri ya anthu, unalemeretsa mafumu a pa dziko lapansi ndi cuma cako cocuruka ndi malonda ako.

Ezekieli 27

Ezekieli 27:28-36