Ezekieli 27:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

nuti kwa Turo, Iwe wakukhala polowera m'nyanja, wakucita malonda ndi mitundu ya anthu m'zisumbu zambiri, atero Ambuye Yehova, Iwe, Turo, wati, Ine ndine wokongola wangwiro.

Ezekieli 27

Ezekieli 27:2-4