Ezekieli 26:19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti atero Ambuye Yehova, Pamene ndikusandutsa mudzi wapasuka, ngati midzi yosakhalamo anthu, ndi kukukweretsera nyanja, nadzakumiza madzi akuru;

Ezekieli 26

Ezekieli 26:15-21