Ezekieli 24:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wobadwa ndi munthu iwe, sikudzakhala kodi tsiku loti ndiwacotsera mphamvu yao, cimwemwe cao copambana, cowakonda m'maso mwao, ndi cokhumbitsa mtima wao, ana ao amuna ndi akazi,

Ezekieli 24

Ezekieli 24:16-27