Ezekieli 24:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi zilemba zanu zidzakhala pamitu panu, ndi nsapato zanu ku mapazi anu, simudzacita cisoni kapena kulira, koma mudzaonda ndi mphulupulu zanu, ndi kubulirana wina ndi mnzace.

Ezekieli 24

Ezekieli 24:16-27