Ezekieli 22:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wobadwa ndi munthu iwe, nyumba ya Israyeli yandikhalira mphala; onsewo ndiwo mkuwa, ndi seta, ndi citsulo, ndi ntobvu, m'kati mwa ng'anjo; ndiwo mphala zasiliva.

Ezekieli 22

Ezekieli 22:15-26