Ezekieli 20:44 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

M'mwemo mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova nditacita nanu cifukwa ca dzina langa, si monga mwa njira zanu zoipa, kapena monga mwa macitidwe anu obvunda, nyumba ya Israyeli inu, ati Ambuye Yehova.

Ezekieli 20

Ezekieli 20:42-49