Ezekieli 20:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace wobadwa ndi munthu iwe, lankhula ndi nyumba ya Israyeli, nunene nao, Atero Ambuye Yehova, Mwa icinso atate anu anandicitira mwano pakundilakwira Ine.

Ezekieli 20

Ezekieli 20:19-30