Ezekieli 2:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nati kwa ine, Wobadwa ndi munthu iwe, ndikutumizira kwa ana a Israyeli, kwa mitundu ya anthu opanduka, amene anapandukana nane; iwo ndi makolo ao anandilakwira mpaka lero lomwe.

Ezekieli 2

Ezekieli 2:1-8