Ezekieli 18:2-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Mutani inu ndi kunena mwambi uwu za dziko la Israyeli, wakuti, Atate adadya mphesa zosacha, ndi mano a ana ayayamira.

3. Pali Ine, ati Ambuye Yehova, simudzaonanso cifukwa ca kunena mwambiwu m'Israyeli.

4. Taonani, miyoyo yonse ndi yanga, monga moyo wa atate momwemonso moyo wa mwana, ndiyo yanga; moyo wocimwawo ndiwo udzafa.

5. Koma munthu akakhala wolungama, nakacita ciweruzo ndi cilungamo,

Ezekieli 18