Ezekieli 16:51 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ngakhale Samariya sanacita theka la zocimwa zako, koma unacurukitsa zonyansa zako kuwaposa iwowa, ndi kuika abale ako olungama ndi zonyansa zako zonse unazicita.

Ezekieli 16

Ezekieli 16:42-61