Ezekieli 16:27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Taona tsono, ndakutambasulira dzanja langa, ndi kucepsa gawo lako la cakudya, ndi kukupereka ku cifuniro ca iwo akudana nawe, kwa ana akazi a Afilisti akucita manyazi ndi njira yako yoipa.

Ezekieli 16

Ezekieli 16:23-35