Ezekieli 14:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Likandicimwira dziko ndi kucita monyenga, ndipo ndikalitambasulira dzanja langa, ndi kulityolera mcirikizo wace, ndiwo mkate, ndi kulitumizira njala, ndi kulidulira munthu ndi nyama,

Ezekieli 14

Ezekieli 14:4-14