Ezekieli 13:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cifukwa cace atero Ambuye Yehova, Ndidzalithithimula ndi mkuntho m'ukali wanga; ndipo lidzabvumbidwa ndi mvula yaikuru mu mkwiyo wanga, ndi matalala akuru adzalitha m'ukali wanga.

Ezekieli 13

Ezekieli 13:12-16