Ezara 9:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kodi tidzabwereza kuphwanya malamulo anu, ndi kukwatana nayo mitundu ya anthu ocita zonyansa izi? Simudzakwiya nafe kodi mpaka mwatitha, ndi kuti pasakhale otsala kapena akupulumuka?

Ezara 9

Ezara 9:12-15