Ezara 8:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo ndinalalikira cosala komweko ku mtsinje wa Ahava, kuti tidzicepetse pamaso pa Mulungu wathu, kumfunsa ationetsere njira yolunjika ya kwa ife, ndi ang'ono athu, ndi cuma cathu conse.

Ezara 8

Ezara 8:14-27