Ezara 7:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ali yense wosacita lamulo la Mulungu wako, ndi lamulo la mfumu, mlandu umtsutse msanga, ngakhale kumupha, kapena kumpitikitsa m'dziko, kapena kumlanda cuma cace, kapena kummanga m'kaidi.

Ezara 7

Ezara 7:19-28