Ezara 6:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndalamuliranso kuti ali yense adzasintha mau awa, usololedwe mtanda kunyumba kwace, namkweze, nampacike pomwepo; niyesedwe dzala nyumba yace cifukwa ca ici;

Ezara 6

Ezara 6:10-15