Ezara 4:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mfumu nibweza mau kwa Rehumu ciwinda ca malamulo, ndi kwa Simsai mlembi, ndi kwa anzao otsala okhala m'Samariya, ndi otsala tsidya lino la mtsinjewo, Mtendere, ndi nthawi yakuti.

Ezara 4

Ezara 4:13-21