Ezara 2:5-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Ana a Ara, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi awiri kudza asanu.

6. Ana a Pahati Moabu, a ana a Yesuwa ndi Yoabu, zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi atatu kudza khumi ndi awiri.

7. Ana a Elamu, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.

8. Ana a Zatu, mazana asanu ndi anai mphambu makumi anai kudza asanu.

9. Ana a Zakai, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi asanu ndi limodzi.

10. Ana a Bani, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.

11. Ana a Bebai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

Ezara 2