38. Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.
39. Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.
40. Alevi: ana a Yesuwa, ndi Kadimiyeli, ndiwo a ana a Hodariya, makumi asanu ndi awiri mphambu anai.
41. Oyimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.