Ezara 2:38-41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

38. Ana a Pasuru, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.

39. Ana a Harimu, cikwi cimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.

40. Alevi: ana a Yesuwa, ndi Kadimiyeli, ndiwo a ana a Hodariya, makumi asanu ndi awiri mphambu anai.

41. Oyimba: ana a Asafu, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Ezara 2