31. Ana a Elamu wina, cikwi cimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi asanu ndi anai.
32. Ana a Harimu, mazana atatu mphambu makumi awiri.
33. Ana a Lodi, Hadidi, ndi Ono, mazana asanu ndi awiri mphambu makumi awiri kudza asanu.
34. Ana a Yeriko, mazana atatu mphambu makumi anai kudza asanu.
35. Ana a Senai, zikwi zitatu mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.