Ezara 2:21-23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

21. Ana a Betelehemu zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.

22. Anthu a ku Netofa, makumi asanu mphambu asanu ndi mmodzi.

23. Anthu a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

Ezara 2