Ezara 2:17-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

17. Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza atatu.

18. Ana a Yora, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.

19. Ana a Hasumu, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.

20. Ana a Gibara, makumi asanu ndi anai mphambu asanu.

21. Ana a Betelehemu zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.

22. Anthu a ku Netofa, makumi asanu mphambu asanu ndi mmodzi.

23. Anthu a ku Anatoti, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.

24. Ana a Azimaveti, makumi anai mphambu awiri.

Ezara 2