Ezara 2:16-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Ana a Ateri, a Hezekiya, makumi asanu ndi anai mphambu asanu ndi atatu.

17. Ana a Bezai, mazana atatu mphambu makumi awiri kudza atatu.

18. Ana a Yora, zana limodzi mphambu khumi ndi awiri.

19. Ana a Hasumu, mazana awiri mphambu makumi awiri kudza atatu.

20. Ana a Gibara, makumi asanu ndi anai mphambu asanu.

Ezara 2