Ezara 10:29-41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

29. Ndi a ana a Bani: Mesulamu, Makuli, ndi Adaya, Yasubi, ndi Seali, Yeremoti.

30. Ndi a ana a Pahati: Moabu, Adina, ndi Kelali, Benaya, Maseya, Mataniya, Bezaleli, ndi Binui, ndi Manase.

31. Ndi a ana a Harimu: Eliezere, Isiya, Malikiya, Semaya, Simeoni,

32. Benjamini, Maluki, Semariya.

33. A ana a Hasumu: Matenai, Matata. Zabadi, Elifeleti, Yeremai, Manase, Simei.

34. A ana a Bani: Madai, Amiramu, ndi Ueli,

35. Benaya, Bedeya, Kelui,

36. Vaniya, Meremoti, Eliasibi,

37. Mataniya, Matenai, ndi Yasu,

38. ndi Bani, ndi Binui, Simei,

39. ndi Selemiya, ndi Natani, ndi Adaya,

40. Makinadebai, Sasai, Sarai,

41. Azareli, ndi Seleimiya, Semariya,

Ezara 10