Estere 1:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi mamwedwewo anali monga mwa lamulo; panalibe kukakamiza; pakuti mfumu idaikira akulu onse a nyumba yace motero, kuti acite monga momwe akhumba ali yense.

Estere 1

Estere 1:4-18