Eksodo 9:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti nthawi yino ndidzatuma miliri yanga yonse pamtima pako, ndi pa anayamata ako, ndi pa anthu ako; kuti udziwe kuti palibe wina wonga Ine pa dziko lonse lapansi.

Eksodo 9

Eksodo 9:6-18