Eksodo 6:2-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Ndipo Mulungu ananena ndi Mose, nati kwa iye, Ine ndine YEHOV A:

3. ndipo ndinaonekera Abrahamu, Isake ndi Yakobo, Mulungu Wamphamvuyonse; koma sindinadziwika kwa iwo ndi dzina langa YEHOV A.

4. Ndipo ndinakhazikitsanso nao cipangano canga, kuwapatsa dziko la Kanani, dziko la maulendo ao, anali alendo m'mwemo.

Eksodo 6