Eksodo 6:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Akuru a mbumba za makolo ao ndi awa: ana amuna a Rubeni, woyamba wa Israyeli ndiwo: Hanoki ndi Palu, Hezroni, ndi Karmi; amene ndiwo mabanja a Rubeni.

Eksodo 6

Eksodo 6:6-15