Eksodo 40:13-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. Nubveke Aroni cobvala zopatulikazo; ndi kumdzoza, ndi kumpatwa andicitire Ine nchito ya nsembe.

14. Ndipo ubwere nao ana ace amuna ndi kuwabveka maraya am'kati;

15. nuwadzoze, monga unadzoza atate wao, kuti andicitire nchito ya nsembe; ndi kudzozedwa kwao kuwakhalire unsembe wosatha mwa mibadwo yao.

16. Anatero Mose; monga mwa zonse Yehova adamuuza, momwemo anacita.

Eksodo 40